Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

“Khulupililani Yehova Mulungu Wanu”

“Khulupililani Yehova Mulungu Wanu”

Atawopsezedwa, Yehosafati na anthu a ku Yuda anapemphela kwa Yehova kuti awathandize (2 Mbiri 20:12, 13; w14 12/15 23 ¶8)

Yehova analimbikitsa anthu ake na kuwapatsa malangizo omveka bwino (2 Mbiri 20:17)

Yehova anapulumutsa anthu ake cifukwa anamukhulupilila (2 Mbiri 20:21, 22, 27; w21.11 16 ¶7)

Pamene Gogi adzaukila anthu a Yehova pa cisautso cacikulu, awo amene adzapitiliza kukhulupilila Yehova na kudalila anthu amene iye akuwagwilitsa nchito potsogolela, sadzaopa ciliconse.—2 Mbiri 20:20.