Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

NYIMBO 30

Atate Wanga, Mulungu Wanga Ndiponso Bwenzi Langa

Atate Wanga, Mulungu Wanga Ndiponso Bwenzi Langa

(Aheberi 6:10)

  1. 1. Nthawi zina m’dzikoli

    Zinthu zingakhale zovuta.

    Komabe ndizingoti

    Moyo ndi wabwino.

    (KOLASI)

    M’lungu ndi wolungama

    Sadzaiwala ntchito zanga.

    Ali pafupi nane

    Nthawi zonse sanditaya.

    Iye adzandipatsa

    Zonse zomwe ndifunikira.

    Ndi Atate, Ndi Mulungu,

    Bwenzi langa.

  2. 2. Panopa ndakalamba.

    Tsopano ndi nthawi yovuta

    Koma chiyembekezo

    Changa ndi champhamvu.

    (KOLASI)

    M’lungu ndi wolungama

    Sadzaiwala ntchito zanga.

    Ali pafupi nane

    Nthawi zonse sanditaya.

    Iye adzandipatsa

    Zonse zomwe ndifunikira.

    Ndi Atate, Ndi Mulungu,

    Bwenzi langa.

(Onaninso Sal. 71:17, 18.)