Pitani ku nkhani yake

Kukhulupirira Mulungu

Chikhulupiriro n’champhamvu kwambiri ndipo chimathandiza munthu kukhala ndi mtendere wam’maganizo panopa komanso chiyembekezo chodalirika cham’tsogolo. Ngati simunakhulupirirepo Mulungu, munasiya kumukhulupirira kapenanso mukufuna kulimbitsa chikhulupiriro chanu, Baibulo lingakuthandizeni.

TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO

Yobu—“Sindidzasiya Kukhala Ndi Mtima Wosagawanika.”

Kodi nkhani ya Yobu ingatithandize bwanji tikakumana ndi mavuto kapena mayesero omwe angayese chikhulupiriro chathu?

TSANZIRANI CHIKHULUPIRIRO CHAWO

Yobu—“Sindidzasiya Kukhala Ndi Mtima Wosagawanika.”

Kodi nkhani ya Yobu ingatithandize bwanji tikakumana ndi mavuto kapena mayesero omwe angayese chikhulupiriro chathu?

Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo—Amuna ndi Akazi Otchulidwa M’Baibulo