Austria
Akuluakulu a Tauni Ina ku Austria Anachita Mwambo Wokumbukira a Mboni 31 Omwe Anazunzidwa Komanso Kuphedwa mu Ulamuliro wa Chipani cha Nazi
Chikwangwani cha ku Techelsberg chinakonzedwa pokumbukira a Mboni za Yehova omwe anazunzidwa ndi a chipani cha Nazi pa nthawi ya Nkhondo Yachiwiri ya Padziko Lonse.
Chikwangwani Chachikumbutso Chinaikidwa Pokumbukira wa Mboni Amene Anaphedwa ndi a Chipani cha Nazi
Gabriele Votava ndi amene anali mlendo wolemekezeka pamwambo wokumbukira Gerhard Steinacher, yemwe anali wa Mboni za Yehova ndipo anaphedwa ali ndi zaka 19 chifukwa chokana kulowa usilikali.
A Mboni za Yehova Analandira Ulemu Pamwambo Wokumbukira Anthu Amene Anazunzidwa M’ndende ya Gusen
Pa April 13, 2014, Anaika chipilala chokumbukira anthu 450 Mboni amene anamangidwa ndi chipani cha Nazi m’ndende ya Mauthausen ndi Gusen ku Austria.