Pitani ku nkhani yake

Sri Lanka

 

2019-01-09

SRI LANKA

Msonkhano Wapadera Woyamba Kuchitikira ku Sri Lanka

A Mboni za Yehova masauzande ambiri ochokera m’mayiko 7 anakumana ndi abale ndi alongo awo auzimu ku Colombo pamsonkhano wapadera, ndipo umenewu unali woyamba kuchitikira ku Sri Lanka.

2016-08-25

SRI LANKA

A Mboni za Yehova Anathandiza Anthu M’dziko la Sri Lanka Mutagwa Chimvula Choopsa

Patangodutsa zaka 12 kuchokera pamene ku Sri Lanka kunachitika tsunami, m’dzikoli munachitikanso ngozi ina ndipo a Mboni za Yehova anathandiza anthu omwe anakhudzidwa.