Pitani ku nkhani yake

Uzbekistan

 

A Mboni za Yehova ku Uzbekistan

2018-12-07

UZBEKISTAN

Makhoti Akuluakulu ku Uzbekistan Anagwirizana ndi Zoti a Mboni za Yehova Ali ndi Ufulu Wokhala ndi Mabuku Ofotokoza za Baibulo

Zigamulo zaposachedwapa zomwe makhoti akuluakulu anapanga, zathandiza kuti abale athu asakhale ndi milandu ndipo sakuyenera kupereka chindapusa.

2014-05-29

UZBEKISTAN

Kodi Zinthu Ziyamba Kuwayendera Bwino a Mboni za Yehova ku Uzbekistan?

Zikuonetsa kuti akuluakulu a boma la Uzbekistan, akuyesetsa kuti ayambe kulemekeza ufulu wachibadwidwe wa anthu. A Mboni za Yehova akukhulupiriranso kuti posachedwapa, akuluakulu a boma akhoza kuvomereza kuti alembetse mipingo yawo yatsopano.