Pitani ku nkhani yake

KODI BAIBULO LIMAPHUNZITSA CHIYANI KWENIKWENI? (ZOKUTHANDIZANI POPHUNZIRA)

Kodi Tilidi ‘M’masiku Otsiriza’? (Gawo 2)

Kodi Baibulo limanena kuti pali zinthu zina zabwino zimene zizichitika ‘m’masiku otsiriza’ ano? Kodi ndi zinthu zabwino ziti zimene zidzachitike masiku otsiriza akadzatha? Taonani

zimene Baibulo limanena pa nkhaniyi.