Pitani ku nkhani yake

KODI BAIBULO LIMAPHUNZITSA CHIYANI KWENIKWENI?(ZOKUTHANDIZANI POPHUNZIRA)

Muziona Moyo Ngati Mmene Mulungu Amauonera (Gawo 2)

Mfundozi zachokera m’mutu 13 wa buku lakuti Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni?

Onani zimene Baibulo limaphunzitsa pa nkhani yogwiritsa ntchito magazi molakwika. Komanso onani njira imodzi yokha yoyenera kugwiritsa ntchito magazi yomwe ingapulumutse moyo wathu.