Pitani ku nkhani yake

Zoti Muchite Pophunzira Baibulo

Pewani Kulakalaka Zinthu Zoipa

Werengani nkhani ya Davide ndi Bati-seba kuti muone zimene mungaphunzirepo. Koperani nkhaniyi, iwerengeni m’Baibulo, ndipo muiganizire mozama n’kuona mmene ingakuthandizireni.