Pitani ku nkhani yake

Zoti Muchite Pophunzira Baibulo

Pewani Mizimu Yoipa

Phunzirani zimene Baibulo limanena pa nkhani ya kupewa mizimu yoipa. Koperani nkhani ya m’Baibuloyi, iwerengeni, ndipo muiganizire mozama n’kuona mmene ingakuthandizireni.