Pitani ku nkhani yake

Imbirani Yehova Nyimbo

Imbirani Yehova Nyimbo

Dulani zithunzizi ndi kuziika malo amodzi potsatira malangizo ndipo kenako imbirani Yehova komanso loweza nyimbo ya mutu wakuti “Dzina Lanu Ndinu Yehova.”

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Inu Ndinu Yehova (Nyimbo 2)

Tamandani dzina lokwezeka la Yehova poimba nyimboyi.

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.