Pitani ku nkhani yake

ZITHUNZI ZOFOTOKOZA NKHANI ZA M’BAIBULO

Aisiraeli Anapanga Mwana wa Ng’ombe Wagolide

Werengani nkhani yofotokoza za Aroni mchimwene wake wa Mose, pamene anachimwa chifukwa chothandiza Aisiraeli kupanga fano la mwana wa ng’ombe wagolide. Werengani nkhaniyi pa Intaneti kapena patsamba limene mwasindikiza.