Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Kodi Mulungu Amamvetsera Mapemphero Onse?

Kodi Mulungu Amamvetsera Mapemphero Onse?

Mulungu amafuna kuti anthu amitundu yonse azilankhula naye kudzera m’pemphero. Koma kodi Mulungu amamvetsera kapena kuvomereza mapemphero onse?