Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

NYIMBO 50

Pemphero Langa Losonyeza Kudzipereka

Pemphero Langa Losonyeza Kudzipereka

(Mateyu 22:37)

  1. 1. Tengani mtima wanga

    Kuti ndikukondeni.

    Tengani mawu anga

    Ndizikuimbirani.

  2. 2. Tengani mapaziwa

    Ndikutumikireni.

    Tengani chuma changa

    Sindingakumaneni.

  3. 3. Tengani moyo wanga.

    Ndikufuna ndichite

    Zimene mumafuna.

    Ndikusangalatseni.