Pitani ku nkhani yake

Chionetsero cha Baibulo Cholemekeza Dzina la Mulungu

Chionetsero cha Baibulo Cholemekeza Dzina la Mulungu

Kuchokera mu 2013, pamene tinatsegulira malo athu oonetsera Mabaibulo osiyanasiyana, takhala tikulandira Mabaibulo akale ndiponso ofunika kwambiri. Tinapatsidwa Mabaibulo monga Complutensian Polyglot ndiponso Mabaibulo akalekale a King James Bible ndi Erasmus’ Greek “New Testament.”