Pitani ku nkhani yake

Phunziro 5: Tiyeni Tikalalikire

Phunziro 5: Tiyeni Tikalalikire

Kodi Sofiya watenga zonse zofunika popita kolalikira?

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Pangani Chikwama cha mu Utumiki

Kodi mumafunika kutenga chiyani popita kolalikira? Tsambali lingakuthandizeni kuti muzitenga chikwama popita mu utumiki.

ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Timapepala Tazithunzi Tofunika Kusunga!

Mungagwiritsire ntchito timapepalati kudziwa malo omwe mumawerenga m’mabuku anu!

MAVIDIYO

Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.