Pitani ku nkhani yake

Timapepala Tazithunzi Tofunika Kusunga!

Timapepala Tazithunzi Tofunika Kusunga!

Dulani timapepalati tomwe mungaphunzirepo zinazake.

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Muzipemphera Nthawi Iliyonse

Vidiyoyi ndi yoti mukhoza kuipanga dawunilodi ndipo imaphunzitsa ana nthawi komanso malo amene angapemphere kwa Yehova.

KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Kuba N’koipa

Kodi Mulungu amakuona bwanji kuba? Werengani Ekisodo 20:15. Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zambiri limodzi ndi Kalebe.

KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Tiyeni Tikalalikire

Kodi Sofiya watenga zonse zofunika popita kolalikira? Onerani vidiyoyi kuti mudziwe zimene inunso muyenera kutenga popita kolalikira.

KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Uzipempha Mwaulemu Ndiponso Uzithokoza

Kalebe waphunzira kuti kupempha mwaulemu ndiponso kuthokoza ndi kofunika kwambiri.

KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Kupatsa N’kwabwino

Pali zambiri zimene mungachite kuti muthandize ena. Kodi mukuganiza kuti mungachite chiyani?

KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Uzikhala Waukhondo

Yehova amaika chilichonse pamalo oyenera. Onani zimene nanunso mungachite kuti muzikhala aukhondo