Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Muziphunzira Kuti Mukhale Olimba

Muziphunzira Kuti Mukhale Olimba

Pangani Dawunilodi:

  1. 1. Kungoyambiratu tili makanda.

    Tinkaphunzira komanso kumazimvetsa.

    N’sanagone bambo ankawerenga.

    Pano ndakula ndimawerengabe ndekha.

    Ndipo ndikafatsa ndimatengatu bukulo.

    Ndimakumbukira zomwe n’nawerenga kuti n’khale wolimba.

    (KOLASI)

    Muziphunzira,

    Udzalimba ngati mtengo wa m’madzi.

    Muziphunzira.

    Zinthu zonsetu zidzakuyendera.

    Muziphunzira.

    Monga mtengo wa mizu yakuya.

    Muziphunzira.

    Udzakula n’kumaona zinthu zonse.

  2. 2. Ndingatani anzanga akandifunsa.

    Za zinthu zomwe ndimazikhulupirira.

    Zimenezitu sizingandivute.

    Kuyambira ndili mwana ndinkaphunzira.

    Ndipo ndikafatsa ndimatengatu bukulo.

    Ndimakumbukira zomwe n’nawerenga kuti n’khale wolimba.

    (KOLASI)

    Muziphunzira,

    Udzalimba ngati mtengo wa m’madzi.

    Muziphunzira.

    Zinthu zonsetu zidzakuyendera.

    Muziphunzira.

    Monga mtengo wa mizu yakuya.

    Muziphunzira.

    Udzakula n’kumaona zinthu zonse.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Zomwe ndimawerenga

    Ndizigwiritsa ntchito

    Kuthandiza ena komanso kuwalimbikitsa.

    (KOLASI)

    Muziphunzira.

    Muziphunzira.

    Muziphunzira.

    Muziphunzira.

    Muziphunzira.

    Udzalimba ngati mtengo wa m’madzi.

    Muziphunzira.

    Zinthu zonsetu zidzakuyendera

    Muziphunzira,

    Monga mtengo wa mizu yakuya.

    Muziphunzira.

    Udzakula n’kumaona zinthu zonse.